Danieli 5:1 - Buku Lopatulika1 Mfumu Belisazara anakonzera anthu ake aakulu chikwi chimodzi madyerero aakulu, namwa vinyo pamaso pa chikwicho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mfumu Belisazara anakonzera anthu ake akulu chikwi chimodzi madyerero akulu, namwa vinyo pamaso pa chikwicho. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tsiku lina mfumu Belisazara anakonza phwando lalikulu la akalonga ake 1,000 ndipo anamwa vinyo pamodzi ndi iwo. Onani mutuwo |