Danieli 11:29 - Buku Lopatulika29 Pa nthawi yoikika adzabwera, nadzalowa kumwera; koma sikudzakhala monga nthawi yoyamba ija, kapena yotsirizayi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Pa nthawi yoikika adzabwera, nadzalowa kumwera; koma sikudzakhala monga nthawi yoyamba ija, kapena yotsirizayi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 “Patapita nthawi mfumu ya kumpoto idzabwereranso kummwera koma sidzapambana monga inachitira kale. Onani mutuwo |