Danieli 11:19 - Buku Lopatulika19 Pamenepo adzatembenuzira nkhope yake kumalinga a dziko lakelake; koma adzakhumudwa, nadzagwa osapezedwanso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Pamenepo adzatembenuzira nkhope yake kumalinga a dziko lakelake; koma adzakhumudwa, nadzagwa osapezedwanso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Zikadzatha izi, mfumu idzabwerera ku malo otetezedwa a dziko la kwawo koma idzapunthwa ndi kugwa osapezekanso. Onani mutuwo |