Danieli 10:8 - Buku Lopatulika8 Momwemo ndinatsala ndekha, ndipo ndinaona masomphenya aakuluwa, koma wosakhala ndi mphamvu ine; pakuti kukoma kwanga kunasandulika chivundi mwa ine, wosakhalanso ndi chimphamvu ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Momwemo ndinatsala ndekha, ndipo ndinaona masomphenya akuluwa, koma wosakhala ndi mphamvu ine; pakuti kukoma kwanga kunasandulika chivundi mwa ine, wosakhalanso ndi chimphamvu ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Choncho ndinatsala ndekha, ndikuonetsetsa masomphenya a ulemererowa. Ndiye nkhope yanga inasinthika, ndinalefuka, ndipo ndinalibenso mphamvu. Onani mutuwo |