Danieli 10:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo atanena ndi ine monga mwa mau awa, ndinaweramitsa nkhope yanga pansi ndi kukhala duu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo atanena ndi ine monga mwa mau awa, ndinaweramitsa nkhope yanga pansi ndi kukhala duu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Pa nthawi yomwe ankanena izi kwa ine, ndinazolika nkhope yanga pansi kusowa chonena. Onani mutuwo |