Danieli 1:18 - Buku Lopatulika18 Atatha masiku inanenawo mfumu kuti alowe nao, mkulu wa adindo analowa nao pamaso pa Nebukadinezara. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Atatha masiku inanenawo mfumu kuti alowe nao, mkulu wa adindo analowa nao pamaso pa Nebukadinezara. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ndipo kumapeto kwa masiku amene mfumu inayika kuti adzaonetse anyamatawa ku nyumba yake, mkulu wa nduna za mfumu uja anawapereka iwo kwa Nebukadinezara. Onani mutuwo |