Amosi 6:2 - Buku Lopatulika2 Pitani ku Kaline, nimuone; kuchokera komweko mupite ku Hamati wamkulu mutsikire ku Gati wa Afilisti; kodi awo ndi okoma koposa maufumu ano? Kapena malire ao aposa malire anu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pitani ku Kaline, nimuone; kuchokera komweko mupite ku Hamati wamkulu mutsikire ku Gati wa Afilisti; kodi awo ndi okoma koposa maufumu ano? Kapena malire ao aposa malire anu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pitani ku mzinda wa Kaline mukaone. Mupitenso ku Hamati mzinda wotchuka uja, tsono mutsikire ku Gati kwa Afilisti. Kodi Aisraelenu mukupambana anthu a mafumu ameneŵa? Kodi kapena dziko lao nlalikulu kupambana lanu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Pitani ku mzinda wa Kaline mukawuyangʼane; mukapitenso ku Hamati-raba mzinda waukulu uja, ndipo mukatsikirenso ku Gati kwa Afilisti. Kodi mizinda imeneyi ndi yopambana maufumu anu awiriwa? Kodi dziko lawo ndi lalikulu kupambana lanu? Onani mutuwo |