Amosi 5:4 - Buku Lopatulika4 Pakuti atero Yehova kwa nyumba ya Israele, Mundifunefune Ine, ndipo mudzakhala ndi moyo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Pakuti atero Yehova kwa nyumba ya Israele, Mundifunefune Ine, ndipo mudzakhala ndi moyo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mau a Chauta ouza banja la Israele ndi aŵa: “Muchite zimene Ine ndifuna, kuti mukhalebe ndi moyo, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Zimene Yehova akunena kwa nyumba ya Israeli ndi izi: “Mundifunefune kuti mukhale ndi moyo; Onani mutuwo |