Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Akolose 3:7 - Buku Lopatulika

7 zimene munayendamo inunso kale, pamene munakhala ndi moyo wanu m'menemo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 zimene munayendamo inunso kale, pamene munakhala ndi moyo wanu m'menemo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Inunso kale makhalidwe anu anali omwewo, munkachita zomwezo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Inunso kale munkachita zomwezi, mʼmoyo wanu wakale uja.

Onani mutuwo Koperani




Akolose 3:7
7 Mawu Ofanana  

Pakuti pamene tinali m'thupi, zilakolako za machimo, zimene zinali mwa chilamulo, zinalikuchita m'ziwalo zathu, kuti zibalire imfa zipatso.


Ndipo ena a inu munali otere; koma munasambitsidwa, koma munayeretsedwa, koma munayesedwa olungama, m'dzina la Ambuye Yesu Khristu, ndi mwa Mzimu wa Mulungu wathu.


zimene munayendamo kale, monga mwa mayendedwe a dziko lapansi lino, monga mwa mkulu wa ulamuliro wa mlengalenga, wa mzimu wakuchita tsopano mwa ana a kusamvera;


Ndipo inu, pokhala akufa m'zolakwa ndi kusadulidwa kwa thupi lanu, anakupatsani moyo pamodzi ndi Iye, m'mene adatikhululukira ife zolakwa zonse;


Pakuti kale ifenso tinali opusa, osamvera, onyengeka, akuchitira ukapolo zilakolako ndi zokondweretsa za mitundumitundu, okhala m'dumbo ndi njiru, odanidwa, odana wina ndi mnzake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa