Akolose 3:14 - Buku Lopatulika14 koma koposa izi zonse khalani nacho chikondano, ndicho chomangira cha mtima wamphumphu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 koma koposa izi zonse khalani nacho chikondano, ndicho chomangira cha mtima wamphumphu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Kuwonjezera pa zonsezi muzikhala ndi chikondi, pakuti nchimene chimamanga zonse m'chigwirizano chathunthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ndipo kuwonjezera pa zonsezi valani chikondi, chimene chimangirira zonsezi pamodzi mu mgwirizano wangwiro. Onani mutuwo |