Akolose 2:6 - Buku Lopatulika6 Chifukwa chake monga momwe munalandira Khristu Yesu Ambuye, muyende mwa Iye, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Chifukwa chake monga momwe munalandira Khristu Yesu Ambuye, muyende mwa Iye, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tsono popeza kuti mudavomereza kuti Khristu Yesu ndi Mbuye wanu, moyo wanu wonse ukhale wolunzana naye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Tsono popeza munavomereza Khristu Yesu kukhala Ambuye anu, mupitirire kukhala mwa Iyeyo. Onani mutuwo |