Ahebri 5:8 - Buku Lopatulika8 angakhale anali Mwana, anaphunzira kumvera ndi izi adamva kuwawa nazo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 angakhale anali Mwana, anaphunzira kumvera ndi izi adamva kuwawa nazo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Motero Yesu, ngakhale anali Mwana wa Mulungu, adaphunzira kumvera pakumva zoŵaŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ngakhale Iye anali Mwana wa Mulungu anaphunzira kumvera pomva zowawa. Onani mutuwo |