Ahebri 13:16 - Buku Lopatulika16 Koma musaiwale kuchitira chokoma ndi kugawira ena; pakuti nsembe zotere Mulungu akondwera nazo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Koma musaiwale kuchitira chokoma ndi kugawira ena; pakuti nsembe zotere Mulungu akondwera nazo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Musanyozere kumachita zachifundo ndi kumathandizana, chifukwa nsembe zotere zimakondweretsa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndipo musayiwale kumachita zabwino ndi kuthandiza ena, pakuti Mulungu amakondwera ndi nsembe zotere. Onani mutuwo |