Ahebri 13:10 - Buku Lopatulika10 Tili nalo guwa la nsembe, limene iwo akutumikira chihema alibe ulamuliro wa kudyako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Tili nalo guwa la nsembe, limene iwo akutumikira chihema alibe ulamuliro wa kudyako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ife tili ndi guwa, ndipo ansembe otumikira m'chihema chachipembedzo cha Ayuda saloledwa kudyako zoperekedwa pamenepo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ife tili ndi guwa lansembe, ndipo ansembe otumikira mʼtenti cha Ayuda, saloledwa kudya zochokera pamenepo. Onani mutuwo |