Ahebri 12:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti talingirirani Iye amene adapirira ndi ochimwa otsutsana naye kotere, kuti mungaleme ndi kukomoka m'moyo mwanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti talingirirani Iye amene adapirira ndi ochimwa otsutsana naye kotere, kuti mungaleme ndi kukomoka m'moyo mwanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Muziganiza za Iye amene adapirira udani waukulu chotere wochokera kwa anthu ochimwa, kuti musafookere ndi kutaya mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Muzilingalira za Iye amene anapirira udani waukulu chotere wochokera kwa anthu ochimwa, kuti musafowoke ndi kutaya mtima. Onani mutuwo |