Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Ahebri 11:18 - Buku Lopatulika

18 amene kudanenedwa za iye, kuti, Mwa Isaki mbeu yako idzaitanidwa:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 amene kudanenedwa za iye, kuti, Mwa Isaki mbeu yako idzaitanidwa:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Za mwana ameneyu Mulungu anali atanena kuti, “Mwa Isaki udzakhala ndi zidzukulu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Za mwana ameneyu Mulungu anamuwuza iye kuti, “Zidzukulu zako zidzachokera mwa Isake.”

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 11:18
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Mulungu anati, Koma Sara mkazi wako adzakubalira iwe mwana wamwamuna; ndipo udzamutcha dzina lake Isaki; ndipo ndidzalimbikitsa naye pangano langa, kuti likhale pangano la nthawi zonse, la ku mbeu zake za pambuyo pake.


Ndipo Mulungu anati kwa Abrahamu, Usaipidwe nao, chifukwa cha mnyamatayo, ndi chifukwa cha mdzakazi wako; momwe monse akunenera iwe Sara umvere iwe mau ake; chifukwa kuti mwa Isaki zidzaitanidwa mbeu zako.


kapena chifukwa ali mbeu ya Abrahamu, siali onse ana; koma anati, Mwa Isaki, mbeu yako idzaitanidwa.


Kale Mulungu analankhula ndi makolo mwa aneneri m'manenedwe ambiri ndi mosiyanasiyana,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa