Ahebri 11:18 - Buku Lopatulika18 amene kudanenedwa za iye, kuti, Mwa Isaki mbeu yako idzaitanidwa: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 amene kudanenedwa za iye, kuti, Mwa Isaki mbeu yako idzaitanidwa: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Za mwana ameneyu Mulungu anali atanena kuti, “Mwa Isaki udzakhala ndi zidzukulu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Za mwana ameneyu Mulungu anamuwuza iye kuti, “Zidzukulu zako zidzachokera mwa Isake.” Onani mutuwo |