Afilipi 4:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo mtendere wa Mulungu wakupambana chidziwitso chonse, udzasunga mitima yanu ndi maganizo anu mwa Khristu Yesu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo mtendere wa Mulungu wakupambana chidziwitso chonse, udzasunga mitima yanu ndi maganizo anu mwa Khristu Yesu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Pamenepo mtendere wochokera kwa Mulungu, umene uli wopitirira nzeru zonse za anthu, udzasunga bwino mitima yanu ndi maganizo anu mwa Khristu Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndipo mtendere wa Mulungu, umene upambana nzeru zonse udzasunga bwino mitima yanu ndi maganizo anu mwa Khristu Yesu. Onani mutuwo |