Afilipi 4:19 - Buku Lopatulika19 Koma Mulungu wanga adzakwaniritsa chosowa chanu chilichonse monga mwa chuma chake mu ulemerero mwa Khristu Yesu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Koma Mulungu wanga adzakwaniritsa chosowa chanu chilichonse monga mwa chuma chake m'ulemerero mwa Khristu Yesu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Mulungu wanga ali ndi chuma chochuluka, ndipo mwa Khristu Yesu adzakupatsani zonse zimene mukusoŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ndipo Mulungu wanga adzakwaniritsa zosowa zanu monga mwa chuma chake chaulemerero mwa Khristu Yesu. Onani mutuwo |