Afilipi 2:26 - Buku Lopatulika26 popeza anali wolakalaka inu nonse, navutika mtima chifukwa mudamva kuti anadwala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 popeza anali wolakalaka inu nonse, navutika mtima chifukwa mudamva kuti anadwala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Tsonotu akukulakalakani nonsenu, ndipo ndi wokhumudwa podziŵa kuti inu mudamva zoti iye ankadwala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Pakuti akukulakalakani nonsenu ndipo akusauka mu mtima chifukwa munamva kuti akudwala. Onani mutuwo |