Afilipi 1:5 - Buku Lopatulika5 chifukwa cha chiyanjano chanu chakuthandizira Uthenga Wabwino, kuyambira tsiku loyambalo, kufikira tsopano lino; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 chifukwa cha chiyanjano chanu chakuthandizira Uthenga Wabwino, kuyambira tsiku loyambalo, kufikira tsopano lino; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndiyeneradi kuthokoza chifukwa mwakhala mukugwirizana nane ndi kundithandiza kufalitsa Uthenga Wabwino, kuchokera tsiku limene mudayamba kukhulupirira mpaka tsopano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 chifukwa mwakhala mukundithandiza polalikira Uthenga Wabwino kuyambira tsiku loyamba mpaka tsopano. Onani mutuwo |