Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Aefeso 6:7 - Buku Lopatulika

7 akuchita ukapolo ndi kuvomereza mtima, monga kutumikira Ambuye Yesu Khristu, si anthu ai;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 akuchita ukapolo ndi kuvomereza mtima, monga kutumikira Ambuye Yesu Khristu, si anthu ai;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Muzitumikira mosangalala, ngati kuti mukutumikira Ambuye, osati anthu chabe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Tumikirani ndi mtima wonse, ngati kuti mukutumikira Ambuye, osati anthu.

Onani mutuwo Koperani




Aefeso 6:7
8 Mawu Ofanana  

Ndipo inu mudziwa kuti ndi mphamvu zanga zonse ndatumikira atate wanu.


Pamenepo anyamata ake anasendera, nanena naye, nati, Atate wanga, mneneri akadakuuzani chinthu chachikulu, simukadachichita kodi? Koposa kotani nanga ponena iye, Samba, nukonzeke?


Koma ayamikidwe Mulungu, kuti ngakhale mudakhala akapolo a uchimo, tsopano mwamvera ndi mtima makhalidwe aja a chiphunzitso chimene munaperekedweracho;


Chifukwa chake mungakhale mudya, mungakhale mumwa, mungakhale muchita kanthu kena, chitani zonse ku ulemerero wa Mulungu.


chilichonse mukachichita, gwirani ntchito mochokera mumtima, monga kwa Ambuye, osati kwa anthu ai;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa