Aefeso 6:7 - Buku Lopatulika7 akuchita ukapolo ndi kuvomereza mtima, monga kutumikira Ambuye Yesu Khristu, si anthu ai; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 akuchita ukapolo ndi kuvomereza mtima, monga kutumikira Ambuye Yesu Khristu, si anthu ai; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Muzitumikira mosangalala, ngati kuti mukutumikira Ambuye, osati anthu chabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Tumikirani ndi mtima wonse, ngati kuti mukutumikira Ambuye, osati anthu. Onani mutuwo |