Aefeso 5:8 - Buku Lopatulika8 pakuti kale munali mdima, koma tsopano muli kuunika mwa Ambuye; yendani monga ana a kuunika, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 pakuti kale munali mdima, koma tsopano muli kuunika mwa Ambuye; yendani monga ana a kuunika, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Inunso kale mudaali mu mdima, koma tsopano muli m'kuŵala, popeza kuti ndinu ao a Ambuye. Tsono muziyenda ngati anthu okhala m'kuŵala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Pajatu inu nthawi ina munali mdima, koma tsopano ndinu kuwunika mwa Ambuye. Mukhale ngati ana akuwunika Onani mutuwo |