Aefeso 5:6 - Buku Lopatulika6 Asakunyengeni inu munthu ndi mau opanda pake, pakuti chifukwa cha izi umadza mkwiyo wa Mulungu pa ana a kusamvera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Asakunyengeni inu munthu ndi mau opanda pake, pakuti chifukwa cha izi umadza mkwiyo wa Mulungu pa ana a kusamvera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Munthu wina aliyense asakupusitseni ndi mau onyenga, pakuti zinthu zotere ndizo zimadzetsa ukali wa Mulungu pa anthu omupandukira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Musalole wina akunamizeni ndi mawu opanda pake, pakuti chifukwa cha zinthu ngati izi mkwiyo wa Mulungu ukubwera pa amene samvera. Onani mutuwo |