Aefeso 5:4 - Buku Lopatulika4 kapena chinyanso, ndi kulankhula zopanda pake, kapena zopusa zimene siziyenera; koma makamaka chiyamiko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 kapena chinyanso, ndi kulankhula zopanda pake, kapena zopusa zimene siziyenera; koma makamaka chiyamiko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndiponso musamalankhule zolaula, zopusa, kapena zopandapake, koma muzilankhula zoyamika Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Musamatukwane, kuyankhula zopusa kapena kunena nthabwala zopanda pake, zomwe ndi zosayenera, koma mʼmalo mwake muziyamika. Onani mutuwo |