Aefeso 5:1 - Buku Lopatulika1 Chifukwa chake khalani akutsanza a Mulungu, monga ana okondedwa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Chifukwa chake khalani akutsanza a Mulungu, monga ana okondedwa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsono popeza kuti ndinu ana okondedwa a Mulungu, muziyesa kumtsanzira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Choncho, monga ana okondedwa, tsatirani chitsanzo cha Mulungu. Onani mutuwo |