Aefeso 4:15 - Buku Lopatulika15 koma ndi kuchita zoona mwa chikondi tikakule m'zinthu zonse, kufikira Iye amene ali mutu ndiye Khristu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 koma ndi kuchita zoona mwa chikondi tikakule m'zinthu zonse, kufikira Iye amene ali mutu ndiye Khristu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Kwenikwenitu pakulankhula zoona ndi mtima wachikondi, tizikula pa zonse mwa Khristu. Iye ndiye mutu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Mʼmalo mwake, poyankhula choonadi mwachikondi, tidzakula mu zinthu zonse ndi kukhala thupi la Khristu, amene ndi Mutu, omwe ndi mpingo. Onani mutuwo |