Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Aefeso 2:9 - Buku Lopatulika

9 chosachokera kuntchito, kuti asadzitamandire munthu aliyense.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 chosachokera kuntchito, kuti asadzitamandire munthu aliyense.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Munthu sapulumuka chifukwa cha ntchito zake, kuwopa kuti angamanyade.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 osati ndi ntchito, kuti wina aliyense asadzitamandire.

Onani mutuwo Koperani




Aefeso 2:9
9 Mawu Ofanana  

Koma ngati kuli ndi chisomo, sikulinso ndi ntchito ai; ndipo pakapanda kutero, chisomo sichikhalanso chisomo.


chifukwa kuti pamaso pake palibe munthu adzayesedwa wolungama ndi ntchito za lamulo; pakuti uchimo udziwika ndi lamulo.


Pakuti ngati Abrahamu anayesedwa wolungama chifukwa cha ntchito, iye akhala nacho chodzitamandira; koma kulinga kwa Mulungu ai.


pakuti anawo asanabadwe, kapena asanachite kanthu kabwino kapena koipa, kuti kutsimikiza mtima kwa Mulungu monga mwa kusankha kukhale, si chifukwa cha ntchito ai, koma chifukwa cha wakuitanayo,


Chotero sichifuma kwa munthu amene afuna, kapena kwa iye amene athamanga, koma kwa Mulungu amene achitira chifundo.


amene anatipulumutsa ife, natiitana ife ndi maitanidwe oyera, si monga mwa ntchito zathu, komatu monga mwa chitsimikizo mtima cha Iye yekha, ndi chisomo, chopatsika kwa ife mwa Khristu Yesu nthawi zisanayambe,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa