Aefeso 2:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo inu, anakupatsani moyo, pokhala munali akufa ndi zolakwa, ndi zochimwa zanu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo inu, anakupatsani moyo, pokhala munali akufa ndi zolakwa, ndi zochimwa zanu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Kale inu munali akufa chifukwa cha zolakwa zanu ndi machimo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Kunena za inu, kale munali akufa chifukwa cha zolakwa zanu ndi machimo anu, Onani mutuwo |