Aefeso 1:20 - Buku Lopatulika20 imene anachititsa mwa Khristu, m'mene anamuukitsa kwa akufa, namkhazikitsa padzanja lake lamanja m'zakumwamba, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 imene anachititsa mwa Khristu, m'mene anamuukitsa kwa akufa, namkhazikitsa pa dzanja lake lamanja m'zakumwamba, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 imene Mulungu adaigwiritsa ntchito pamene adaukitsa Khristu kwa akufa, namkhazika ku dzanja lake lamanja m'dziko la Kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 imene inagwira ntchito pamene Mulungu anaukitsa Khristu kwa akufa, namukhazika Iye ku dzanja lake lamanja mʼdziko la kumwamba. Onani mutuwo |