Aefeso 1:12 - Buku Lopatulika12 kuti ife amene tinakhulupirira Khristu kale tikayamikitse ulemerero wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 kuti ife amene tinakhulupirira Khristu kale tikayamikitse ulemerero wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Adafuna kuti ife, amene tinali oyamba kuyembekeza Khristu, tilemekeze ulemerero wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 nʼcholinga chakuti, ife amene tinali oyamba kukhala ndi chiyembekezo mwa Khristu, tiyamike ulemerero wake. Onani mutuwo |