2 Timoteyo 3:5 - Buku Lopatulika5 akukhala nao maonekedwe a chipembedzo, koma mphamvu yake adaikana; kwa iwonso udzipatule. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 akukhala nao maonekedwe a chipembedzo, koma mphamvu yake adaikana; kwa iwonso udzipatule. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Adzasamala maonekedwe ake okha a chipembedzo, nkumakana mphamvu zake. Anthu otere uziŵalewa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Adzakhala ndi maonekedwe achipembedzo koma mphamvu yake ndi kumayikana. Anthu amenewa uziwapewa. Onani mutuwo |