2 Timoteyo 3:1 - Buku Lopatulika1 Koma zindikira ichi, kuti masiku otsiriza zidzafika nthawi zowawitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Koma zindikira ichi, kuti masiku otsiriza zidzafika nthawi zowawitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Udziŵe kuti pa masiku otsiriza kudzafika nthaŵi ya zovuta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Koma dziwa izi: Mʼmasiku otsiriza kudzafika nthawi zoopsa kwambiri. Onani mutuwo |