2 Samueli 5:4 - Buku Lopatulika4 Davide anali ndi zaka makumi atatu polowa iye ufumu wake, nakhala mfumu zaka makumi anai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Davide anali ndi zaka makumi atatu polowa iye ufumu wake, nakhala mfumu zaka makumi anai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Davide anali wa zaka makumi atatu za kubadwa pamene adaloŵa ufumu. Adakhala mu ufumu zaka makumi anai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Davide anali ndi zaka makumi atatu pamene anakhala mfumu, ndipo analamulira zaka makumi anayi. Onani mutuwo |