2 Samueli 4:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo anabwera nao mutu wa Isiboseti kwa Davide ku Hebroni, nanena ndi mfumu, Taonani mutu wa Isiboseti mwana wa Saulo, mdani wanu amene anafuna moyo wanu; Yehova anabwezerera chilango mbuye wanga mfumu lero lino kwa Saulo ndi mbeu yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo anabwera nao mutu wa Isiboseti kwa Davide ku Hebroni, nanena ndi mfumu, Taonani mutu wa Isiboseti mwana wa Saulo, mdani wanu amene anafuna moyo wanu; Yehova anabwezerera chilango mbuye wanga mfumu lero lino kwa Saulo ndi mbeu yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tsono mutu wa Isibosetiwo adapita nawo kwa Davide ku Hebroni. Adauza mfumuyo kuti, “Amfumu, suwu mutu wa Isiboseti, mwana wa Saulo, mdani wanu uja ankafunafuna kukuphaniyu. Lero lino Chauta walipsirira Saulo ndi zidzukulu zake chifukwa cha inu mbuyanga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Iwo anabweretsa mutu wa Isi-Boseti kwa Davide ku Hebroni ndipo anati kwa mfumu, “Nawu mutu wa Isiboseti mwana wa Sauli, mdani wanu, amene anafuna kukuphani. Lero lino Yehova wabwezera mbuye wanga mfumu adani anu, Sauli ndi ana ake.” Onani mutuwo |