2 Samueli 2:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo tsikulo nkhondo inakula ndithu. Ndi Abinere ndi anthu a Israele anathawa pamaso pa anyamata a Davide. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo tsikulo nkhondo inakula ndithu. Ndi Abinere ndi anthu a Israele anathawa pamaso pa anyamata a Davide. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Tsono panali nkhondo yoopsa tsiku limenelo. Abinere pamodzi ndi anthu a ku Israele adagonjetsedwa ndi ankhondo a Davide. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Tsiku limeneli nkhondo yake inali yoopsa kwambiri, ndipo Abineri ndi ankhondo a Israeli anagonjetsedwa ndi ankhondo a Davide. Onani mutuwo |