2 Petro 3:3 - Buku Lopatulika3 ndi kuyamba kuchizindikira ichi kuti masiku otsiriza adzafika onyoza ndi kuchita zonyoza, oyenda monga mwa zilakolako za iwo eni, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 ndi kuyamba kuchizindikira ichi kuti masiku otsiriza adzafika onyoza ndi kuchita zonyoza, oyenda monga mwa zilakolako za iwo eni, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Choyamba mumvetse izi: pa masiku otsiriza kudzafika anthu olalata, otsata zilakolako zao zoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Poyamba mudziwe kuti mʼmasiku otsiriza kudzafika anthu onyoza, adzanyoza ndi kutsata zilakolako zawo zoyipa. Onani mutuwo |