2 Petro 2:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo ambiri adzatsata zonyansa zao; chifukwa cha iwo njira ya choonadi idzanenedwa zamwano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo ambiri adzatsata zonyansa zao; chifukwa cha iwo njira ya choonadi idzanenedwa zamwano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ambiri adzatsata mkhalidwe wodzilekerera ndipo anthu adzanyoza njira ya choona chifukwa cha iwowo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ambiri adzatsata njira zawo zochititsa manyazi ndipo chifukwa cha iwowa, anthu adzanyoza njira ya choonadi. Onani mutuwo |