2 Mafumu 13:2 - Buku Lopatulika2 Nachita choipa pamaso pa Yehova, natsata zolakwa za Yerobowamu mwana wa Nebati, zimene analakwitsa nazo Israele; sanazileke. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Nachita choipa pamaso pa Yehova, natsata zolakwa za Yerobowamu mwana wa Nebati, zimene analakwitsa nazo Israele; sanazileke. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Iyeyo adachita zoipa kuchimwira Chauta. Zoipa zomwe Yerobowamu mwana wa Nebati adachimwitsa nazo Aisraele sadazileke ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iye anachita zoyipa pamaso pa Yehova potsatira machimo a Yeroboamu mwana Nebati amene anachimwitsa nawo Israeli ndipo iye sanawaleke machimowo. Onani mutuwo |