Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Mafumu 10:2 - Buku Lopatulika

2 Tsono ikakufikani inu kalata iyi, popeza muli nao ana a mbuye wanu, muli naonso magaleta ndi akavalo, ndi mizinda yalinga, ndi zida,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Tsono akakufikani inu kalata uyu, popeza muli nao ana a mbuye wanu, muli naonso magaleta ndi akavalo, ndi mudzi walinga, ndi zida,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 “Inu mukusamalira zidzukulu za mbuyanu Ahabu, ndipo muli nawo magaleta, zida zankhondo ndiponso mizinda yamalinga. Nchifukwa chake tsono mukangolandira kalatayi,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 “Inu mukangolandira kalatayi, popeza ana a mbuye wanu ali ndi inu ndiponso muli ndi magaleta ndi akavalo, mzinda wotetezedwa ndi zida zankhondo,

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 10:2
2 Mawu Ofanana  

musankhe wokoma ndi woyenerayo wa ana a mbuye wanu, ndi kumuika pa mpando wachifumu wa atate wake; ndipo muiponyere nkhondo nyumba ya mbuye wanu.


Ndipo anafika kwa mfumu ya Israele ndi kalata, yakuti, Pakulandira kalata iyi, taonani, ndatumiza Naamani mnyamata wanga kwa inu, kuti mumchiritse khate lake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa