2 Akorinto 9:7 - Buku Lopatulika7 Yense achite monga anatsimikiza mtima, si mwa chisoni kapena mokakamiza, pakuti Mulungu akonda wopereka mokondwerera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Yense achite monga anatsimikiza mtima, si mwa chisoni kapena mokakamiza, pakuti Mulungu akonda wopereka mokondwerera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Aliyense apereke monga momwe adatsimikiziratu mumtima mwake, osati ndi chisoni kapena mokakamizidwa, pakuti Mulungu amakonda wopereka mokondwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Munthu aliyense apereke chimene watsimikiza mu mtima mwake kuti apereka, osati monyinyirika kapena mokakamizidwa, pakuti Mulungu amakonda wopereka mokondwera. Onani mutuwo |