2 Akorinto 6:9 - Buku Lopatulika9 monga osadziwika, angakhale adziwika bwino; monga alinkufa, ndipo taonani tili ndi moyo; monga olangika, ndipo osaphedwa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 monga osadziwika, angakhale adziwika bwino; monga alinkufa, ndipo taonani tili ndi moyo; monga olangika, ndipo osaphedwa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Amatiyesa osadziŵika, komabe ndife odziŵika kwambiri. Amatiyesa anthu amene alikufa, komabe onani, tili moyo. Amatiyesa olangidwa, komabe sitidaphedwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Amatiyesa osadziwika komatu ndife odziwika kwambiri. Amatiyesa wooneka ngati tikufa, koma tikupitirirabe ndi moyo, okanthidwa, koma osaphedwa. Onani mutuwo |