2 Akorinto 6:18 - Buku Lopatulika18 ndipo ndidzakhala kwa inu Atate, ndi inu mudzakhala kwa Ine ana aamuna ndi aakazi, anena Ambuye Wamphamvuyonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 ndipo ndidzakhala kwa inu Atate, ndi inu mudzakhala kwa Ine ana aamuna ndi aakazi, anena Ambuye Wamphamvuyonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ndidzakhala Atate anu, inu mudzakhala ana anga aamuna ndi aakazi, akutero Ambuye Mphambe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ndipo “Ndidzakhala Atate anu, ndipo inu mudzakhala ana anga aamuna ndi aakazi, akutero Ambuye, Wamphamvuzonse.” Onani mutuwo |