2 Akorinto 6:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo Khristu avomerezana bwanji ndi Beliyali? Kapena wokhulupirira ali nalo gawo lanji pamodzi ndi wosakhulupirira? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo Khristu avomerezana bwanji ndi Beliyali? Kapena wokhulupirira ali nalo gawo lanji pamodzi ndi wosakhulupirira? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Kodi Khristu nkuvomerezana ndi Satana? Kodi mkhristu ndi mkunja angagaŵanenso chiyani pamodzi? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Pali mgwirizano wanji pakati pa Khristu ndi Beliyali? Kapena munthu wokhulupirira angayanjane bwanji ndi munthu wosakhulupirira? Onani mutuwo |