2 Akorinto 5:17 - Buku Lopatulika17 Chifukwa chake ngati munthu aliyense ali mwa Khristu ali wolengedwa watsopano; zinthu zakale zapita, taonani, zakhala zatsopano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Chifukwa chake ngati munthu aliyense ali mwa Khristu ali wolengedwa watsopano; zinthu zakale zapita, taonani, zakhala zatsopano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Choncho ngati munthu ali mwa Khristu, ngwolengedwa kwatsopano. Zakale zapita, zimene zilipo nzatsopano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Nʼchifukwa chake, ngati munthu aliyense ali mwa Khristu, ndi wolengedwa kwatsopano; zinthu zakale zapita taonani, zakhala zatsopano. Onani mutuwo |