2 Akorinto 4:5 - Buku Lopatulika5 Pakuti tilalikira si za ife tokha, koma Yesu Khristu Ambuye, ndi ife tokha akapolo anu, chifukwa cha Khristu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pakuti tilalikira si za ife tokha, koma Yesu Khristu Ambuye, ndi ife tokha akapolo anu, chifukwa cha Khristu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Motero polalika sitidzilalika tokha, koma timalalika Yesu Khristu, kuti ndiye Ambuye. Ife ndife atumiki anu chabe chifukwa cha Yesuyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Choncho sitilalikira za ife eni, koma Yesu Khristu monga Ambuye, ife ndife atumiki anu chifukwa cha Yesu. Onani mutuwo |