2 Akorinto 11:1 - Buku Lopatulika1 Bwenzi mutandilola pang'ono ndi chopusacho! Komanso mundilole. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Bwenzi mutandilola pang'ono ndi chopusacho! Komanso mundilole. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ndikadakonda kuti mundilekerere pang'ono pa kupusa kwangaku. Tandilekereranipo ndithu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndikukhulupirira kuti mupirira nako pangʼono kupusa kwanga. Chonde tandipirirani! Onani mutuwo |