2 Akorinto 10:6 - Buku Lopatulika6 ndi kukhala okonzeka kubwezera chilango kusamvera konse, pamene kumvera kwanu kudzakwaniridwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndi kukhala okonzeka kubwezera chilango kusamvera konse, pamene kumvera kwanu kudzakwaniridwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndipo inu mutakhala omvera kwenikweni, tili okonzeka kulanga aliyense amene samvera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndipo ife tidzakhala okonzeka kulanga aliyense wosamvera ngati inuyo mutakhala omvera kwenikweni. Onani mutuwo |