2 Akorinto 1:18 - Buku Lopatulika18 Koma Mulungu ali wokhulupirika, kuti mau athu a kwa inu sanakhale eya ndi iai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Koma Mulungu ali wokhulupirika, kuti mau athu a kwa inu sanakhala eya ndi iai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Pali Mulungu woona, ndikulumbira kuti mau athu amene timakuuzani sali “Inde” ndiponso “Ai”. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Koma zoona monga Mulungu ali wokhulupirika, uthenga wathu kwa inu siwakuti, “Inde” nʼkutinso “Ayi.” Onani mutuwo |