1 Yohane 4:5 - Buku Lopatulika5 mwa ichi alankhula monga ochokera m'dziko lapansi, ndipo dziko lapansi liwamvera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 mwa ichi alankhula monga ochokera m'dziko lapansi, ndipo dziko lapansi liwamvera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Aneneri onamawo ndi apansipano, nchifukwa chake zimene amalankhula nzapansipano, ndipo anthu odalira zapansipano amaŵamvera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Aneneri onyengawa ndi ochokera mʼdziko lapansi, nʼchifukwa chake amayankhula za dziko lapansi, ndipo dziko lapansi limawamvera. Onani mutuwo |