1 Yohane 1:8 - Buku Lopatulika8 Tikati kuti tilibe uchimo, tidzinyenga tokha, ndipo mwa ife mulibe choonadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Tikati kuti tilibe uchimo, tidzinyenga tokha, ndipo mwa ife mulibe choonadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tikanena kuti tilibe tchimo, tikudzinyenga, ndipo mwa ife mulibe choona. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Tikanena kuti tilibe tchimo, tikudzinyenga tokha ndipo mwa ife mulibe choonadi. Onani mutuwo |